![](https://www.malawivoice.com/wp-content/uploads/2025/02/1738407906735.jpg)
Usi wati a Malawi ali ndi mtima wa “Khwizi”
Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino, Dr Michael Usi, wati m’dziko muno muli anthu oyipa amene amafuna anzawo adzidutsa muzovuta nthawi zonse. Dr Usi ati pali anthu ena amene akaona mmera wabwino m’munda sakukondwa kaamba koti akufuna anthu m’dziko muno …